×

Iwo anasandutsa Abusa ndi atsogoleri awo a mpingo kukhala Ambuye mowonjezera pa 9:31 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Taubah ⮕ (9:31) ayat 31 in Chichewa

9:31 Surah At-Taubah ayat 31 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Taubah ayat 31 - التوبَة - Page - Juz 10

﴿ٱتَّخَذُوٓاْ أَحۡبَارَهُمۡ وَرُهۡبَٰنَهُمۡ أَرۡبَابٗا مِّن دُونِ ٱللَّهِ وَٱلۡمَسِيحَ ٱبۡنَ مَرۡيَمَ وَمَآ أُمِرُوٓاْ إِلَّا لِيَعۡبُدُوٓاْ إِلَٰهٗا وَٰحِدٗاۖ لَّآ إِلَٰهَ إِلَّا هُوَۚ سُبۡحَٰنَهُۥ عَمَّا يُشۡرِكُونَ ﴾
[التوبَة: 31]

Iwo anasandutsa Abusa ndi atsogoleri awo a mpingo kukhala Ambuye mowonjezera pa Mulungu ndi Messiya, mwana wa Maria, ngati Mulungu pamene iwo adalamulidwa kuti asapembedze wina aliyense koma Mulungu mmodzi yekha basi. Kulibe mulungu wina koma Iye yekha. Kuyamikidwa ndi kulemekezedwa kukhale kwa Iye kuposa zonse zimene adazikhazikitsa mowonjezera pa Iye

❮ Previous Next ❯

ترجمة: اتخذوا أحبارهم ورهبانهم أربابا من دون الله والمسيح ابن مريم وما أمروا, باللغة نيانجا

﴿اتخذوا أحبارهم ورهبانهم أربابا من دون الله والمسيح ابن مريم وما أمروا﴾ [التوبَة: 31]

Khaled Ibrahim Betala
“Awachita ophunzira a za chipembedzo chawo ndi ansembe awo kukhala milungu kusiya Allah (powatsata pa zimene akuwalamula popanda umboni wa Allah). (Amsandutsanso) Mesiya (Isa {Yesu}) mwana wa Mariya (kukhala mulungu); chikhalirecho sadalamulidwe china koma kupembedza Mulungu Mmodzi. Palibe wopembedzedwa mwachoonadi koma Iye, wapatukana ndi zimene akumphatikiza nazozo
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek