×

Ngati inu simudzathandiza Mtumwi, Mulungu adamuthandiza iye pamene anthu osakhulupirira adamupilikitsa, mmodzi 9:40 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Taubah ⮕ (9:40) ayat 40 in Chichewa

9:40 Surah At-Taubah ayat 40 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Taubah ayat 40 - التوبَة - Page - Juz 10

﴿إِلَّا تَنصُرُوهُ فَقَدۡ نَصَرَهُ ٱللَّهُ إِذۡ أَخۡرَجَهُ ٱلَّذِينَ كَفَرُواْ ثَانِيَ ٱثۡنَيۡنِ إِذۡ هُمَا فِي ٱلۡغَارِ إِذۡ يَقُولُ لِصَٰحِبِهِۦ لَا تَحۡزَنۡ إِنَّ ٱللَّهَ مَعَنَاۖ فَأَنزَلَ ٱللَّهُ سَكِينَتَهُۥ عَلَيۡهِ وَأَيَّدَهُۥ بِجُنُودٖ لَّمۡ تَرَوۡهَا وَجَعَلَ كَلِمَةَ ٱلَّذِينَ كَفَرُواْ ٱلسُّفۡلَىٰۗ وَكَلِمَةُ ٱللَّهِ هِيَ ٱلۡعُلۡيَاۗ وَٱللَّهُ عَزِيزٌ حَكِيمٌ ﴾
[التوبَة: 40]

Ngati inu simudzathandiza Mtumwi, Mulungu adamuthandiza iye pamene anthu osakhulupirira adamupilikitsa, mmodzi mwa awiri, pamene iwo adali kuphanga ndipo iye ananena kwa mnzake kuti: Usade nkhawa, ndithudi Mulungu ali nafe. Ndipo Mulungu adatsitsa chisomo chake pa iye ndipo adamulimbikitsa ndi Asirikali omwe sadawaone ndipo Iye adapanga mawu a anthu osakhulupirira kukhala a pansi, ndi a Mulungu kukhala a pamwamba. Ndithudi Mulungu ndi Wamphamvu ndi Wanzeru

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إلا تنصروه فقد نصره الله إذ أخرجه الذين كفروا ثاني اثنين إذ, باللغة نيانجا

﴿إلا تنصروه فقد نصره الله إذ أخرجه الذين كفروا ثاني اثنين إذ﴾ [التوبَة: 40]

❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek