×

Iwo amapembedza zinthu zina, osati Mulungu, zimene sizingathe kuwapweteka kapena kuwathandiza ndipo 10:18 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:18) ayat 18 in Chichewa

10:18 Surah Yunus ayat 18 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 18 - يُونس - Page - Juz 11

﴿وَيَعۡبُدُونَ مِن دُونِ ٱللَّهِ مَا لَا يَضُرُّهُمۡ وَلَا يَنفَعُهُمۡ وَيَقُولُونَ هَٰٓؤُلَآءِ شُفَعَٰٓؤُنَا عِندَ ٱللَّهِۚ قُلۡ أَتُنَبِّـُٔونَ ٱللَّهَ بِمَا لَا يَعۡلَمُ فِي ٱلسَّمَٰوَٰتِ وَلَا فِي ٱلۡأَرۡضِۚ سُبۡحَٰنَهُۥ وَتَعَٰلَىٰ عَمَّا يُشۡرِكُونَ ﴾
[يُونس: 18]

Iwo amapembedza zinthu zina, osati Mulungu, zimene sizingathe kuwapweteka kapena kuwathandiza ndipo amati,“Izi zidzatilankhuliraifekwa Mulungu.” Nena,“Kodi inu mukumuuza Mulungu za zinthu zimene Iye sazidziwa zomwe zili kumwamba kapena pa dziko lapansi? Iye ndi Woyera ndipo akhale wa pamwamba kuposa mafano awo.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ويعبدون من دون الله ما لا يضرهم ولا ينفعهم ويقولون هؤلاء شفعاؤنا, باللغة نيانجا

﴿ويعبدون من دون الله ما لا يضرهم ولا ينفعهم ويقولون هؤلاء شفعاؤنا﴾ [يُونس: 18]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo iwo akupembedza milungu yina kusiya Allah, yomwe singathe kuwapatsa masautso (ngati atasiya kuipembedza) ndiponso siyingathe kuwapatsa chithandizo (ngati atalimbika kuipembedza) ndipo akunena: “Iwo (mafanowo) ndi aomboli athu kwa Allah.” Nena: “Kodi mukumuuza Allah zomwe sakudziwa kumwamba ndi pansi? Wapatukana Allah Ndipo watukuka kuzimene akum’phatikiza nazo.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek