×

Ndipo iwo amene amachitazoipa, malipiroawondioipamofananandizimene adachita. Mnyozo udzawakuta ndipo iwo sadzakhala ndi 10:27 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:27) ayat 27 in Chichewa

10:27 Surah Yunus ayat 27 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 27 - يُونس - Page - Juz 11

﴿وَٱلَّذِينَ كَسَبُواْ ٱلسَّيِّـَٔاتِ جَزَآءُ سَيِّئَةِۭ بِمِثۡلِهَا وَتَرۡهَقُهُمۡ ذِلَّةٞۖ مَّا لَهُم مِّنَ ٱللَّهِ مِنۡ عَاصِمٖۖ كَأَنَّمَآ أُغۡشِيَتۡ وُجُوهُهُمۡ قِطَعٗا مِّنَ ٱلَّيۡلِ مُظۡلِمًاۚ أُوْلَٰٓئِكَ أَصۡحَٰبُ ٱلنَّارِۖ هُمۡ فِيهَا خَٰلِدُونَ ﴾
[يُونس: 27]

Ndipo iwo amene amachitazoipa, malipiroawondioipamofananandizimene adachita. Mnyozo udzawakuta ndipo iwo sadzakhala ndi wina aliyense wowateteza ku chilango chochokera kwa Mulungu. Ndipo nkhope zawo zidzaoneka ngati kuti zidakutidwa ndi mbali ya mdima wa usiku. Iwo adzakhala anthu a kumoto ndipo adzakhala kumeneko nthawi zonse

❮ Previous Next ❯

ترجمة: والذين كسبوا السيئات جزاء سيئة بمثلها وترهقهم ذلة ما لهم من الله, باللغة نيانجا

﴿والذين كسبوا السيئات جزاء سيئة بمثلها وترهقهم ذلة ما لهم من الله﴾ [يُونس: 27]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo amene akolola zoipa (kuchokera m’zochita zawo zoipa) mphoto ya choipa ndiyofanana ndi icho; ndipo kunyozeka kudzawapeza; sadzakhala ndi aliyense wotha kuwateteza ku chilango cha Allah. Nkhope zawo zidzakhala ngati zaphimbidwa ndi zidutswa za usiku wa m’dima, (zidzakhala zakuda kwambiri); awo ndiwo anthu a ku Moto. Iwo mmenemo adzakhala nthawi yaitali
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek