×

Tsiku limene tidzawasonkhanitsa onse, Ife tidzati kwa anthu opembedza mafano: “Khalani m’malo 10:28 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:28) ayat 28 in Chichewa

10:28 Surah Yunus ayat 28 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 28 - يُونس - Page - Juz 11

﴿وَيَوۡمَ نَحۡشُرُهُمۡ جَمِيعٗا ثُمَّ نَقُولُ لِلَّذِينَ أَشۡرَكُواْ مَكَانَكُمۡ أَنتُمۡ وَشُرَكَآؤُكُمۡۚ فَزَيَّلۡنَا بَيۡنَهُمۡۖ وَقَالَ شُرَكَآؤُهُم مَّا كُنتُمۡ إِيَّانَا تَعۡبُدُونَ ﴾
[يُونس: 28]

Tsiku limene tidzawasonkhanitsa onse, Ife tidzati kwa anthu opembedza mafano: “Khalani m’malo mwanu, inu pamodzi ndi mafano anu.” Ife tidzawasiyanitsa wina ndi mnzake ndipo mafano awo adzati kwa iwo: “Sindife amene inu munali kupembedza ayi.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ويوم نحشرهم جميعا ثم نقول للذين أشركوا مكانكم أنتم وشركاؤكم فزيلنا بينهم, باللغة نيانجا

﴿ويوم نحشرهم جميعا ثم نقول للذين أشركوا مكانكم أنتم وشركاؤكم فزيلنا بينهم﴾ [يُونس: 28]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo (akumbutse za) tsiku lomwe tidzawasonkhanitsa onse. Kenako tidzawauza amene ankaphatikiza (Allah ndi mafano kuti): “Imani pompo inu pamodzi ndi aphatikizi anuwo.” Ndipo tidzawasiyanitsa pakati pawo; koma aphatikizi awowo adzati: “Simudali kutipembedza ife (koma mudali kupembedza zilakolako zanu).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek