×

Nena, “Kodi ndani amakupatsani zinthu kuchokera kumwamba ndi padziko lapansi? Kodi ndani 10:31 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:31) ayat 31 in Chichewa

10:31 Surah Yunus ayat 31 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 31 - يُونس - Page - Juz 11

﴿قُلۡ مَن يَرۡزُقُكُم مِّنَ ٱلسَّمَآءِ وَٱلۡأَرۡضِ أَمَّن يَمۡلِكُ ٱلسَّمۡعَ وَٱلۡأَبۡصَٰرَ وَمَن يُخۡرِجُ ٱلۡحَيَّ مِنَ ٱلۡمَيِّتِ وَيُخۡرِجُ ٱلۡمَيِّتَ مِنَ ٱلۡحَيِّ وَمَن يُدَبِّرُ ٱلۡأَمۡرَۚ فَسَيَقُولُونَ ٱللَّهُۚ فَقُلۡ أَفَلَا تَتَّقُونَ ﴾
[يُونس: 31]

Nena, “Kodi ndani amakupatsani zinthu kuchokera kumwamba ndi padziko lapansi? Kodi ndani amene amapereka mphamvu yakumva ndi kuona? Kodi ndani amatulutsa cha moyo kuchokera ku chakufa ndi kutulutsa chakufa kuchokera mu chamoyo? Ndani amene amalamulira zinthu zonse?” Onse adzanena kuti, “Ndi Mulungu.” Nena, “Kodi inu simungaope Mulungu?”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قل من يرزقكم من السماء والأرض أمن يملك السمع والأبصار ومن يخرج, باللغة نيانجا

﴿قل من يرزقكم من السماء والأرض أمن يملك السمع والأبصار ومن يخرج﴾ [يُونس: 31]

Khaled Ibrahim Betala
“Nena: “Kodi ndani akukupatsani (zopatsa) kuchokera kumwamba (povumbwitsa mvula), ndi pansi (pomeretsa mmera)? Nanga ndani amakupatsani kumva ndi kupenya? Nanga ndani amene akutulutsa chamoyo kuchokera m’chakufa, ndi kutulutsa chakufa kuchokera m’chamoyo? Nanga ndani akukonza zinthu zonse?” Anena: “Ndi Allah.” Choncho, nena: “Kodi bwanji simukumuopa?”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek