×

Sizingatheke kuti Korani iyi ikhale yopeka ndiponso kuti siinachokere kwa Mulungu. Koma 10:37 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:37) ayat 37 in Chichewa

10:37 Surah Yunus ayat 37 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 37 - يُونس - Page - Juz 11

﴿وَمَا كَانَ هَٰذَا ٱلۡقُرۡءَانُ أَن يُفۡتَرَىٰ مِن دُونِ ٱللَّهِ وَلَٰكِن تَصۡدِيقَ ٱلَّذِي بَيۡنَ يَدَيۡهِ وَتَفۡصِيلَ ٱلۡكِتَٰبِ لَا رَيۡبَ فِيهِ مِن رَّبِّ ٱلۡعَٰلَمِينَ ﴾
[يُونس: 37]

Sizingatheke kuti Korani iyi ikhale yopeka ndiponso kuti siinachokere kwa Mulungu. Koma iyo imatsimikiza zinthu zonse zimene zidavumbulutsidwa kale ndi kufotokoza Mau a m’buku la Mulungu. Ilo ndi losakaikitsa ndipo ndi lochokera kwa Ambuye wa zolengedwa zonse

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وما كان هذا القرآن أن يفترى من دون الله ولكن تصديق الذي, باللغة نيانجا

﴿وما كان هذا القرآن أن يفترى من دون الله ولكن تصديق الذي﴾ [يُونس: 37]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo sikotheka Qur’an iyi kukhala yopekedwa, yosachokera kwa Allah (monga momwe munenera). Koma (yachokera kwa Allah) kutsimikizira zomwe zidalipo patsogolo pake, ndi kulongosola za buku (lakale). Palibe chikaiko m’menemo (kuti) yachokera kwa Mbuye wa zolengedwa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek