×

Kapena iwo amati “Iye walipeka!” Nena: “Nanunso pekani mutu umodzi wolingana nalo 10:38 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:38) ayat 38 in Chichewa

10:38 Surah Yunus ayat 38 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 38 - يُونس - Page - Juz 11

﴿أَمۡ يَقُولُونَ ٱفۡتَرَىٰهُۖ قُلۡ فَأۡتُواْ بِسُورَةٖ مِّثۡلِهِۦ وَٱدۡعُواْ مَنِ ٱسۡتَطَعۡتُم مِّن دُونِ ٱللَّهِ إِن كُنتُمۡ صَٰدِقِينَ ﴾
[يُونس: 38]

Kapena iwo amati “Iye walipeka!” Nena: “Nanunso pekani mutu umodzi wolingana nalo ndipo itanani amene mungathe kuwaitana osakhala Mulungu ngati muli angwiro!”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: أم يقولون افتراه قل فأتوا بسورة مثله وادعوا من استطعتم من دون, باللغة نيانجا

﴿أم يقولون افتراه قل فأتوا بسورة مثله وادعوا من استطعتم من دون﴾ [يُونس: 38]

Khaled Ibrahim Betala
“Kapena akunena kuti waipeka? Nena: “Tabwerani ndi sura (imodzi) yofanana ndi iyo, ndipo itanani amene mungathe (kuwaitana kuti akuthandizeni) kupatula Allah, ngati inu mukunena zoona (kuti Qur’aniyi waipeka Muhammad {s.a.w}).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek