×

Ndithudi Mulungu salakwira anthu koma kuti anthu eni ake amadzipondereza okha 10:44 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:44) ayat 44 in Chichewa

10:44 Surah Yunus ayat 44 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 44 - يُونس - Page - Juz 11

﴿إِنَّ ٱللَّهَ لَا يَظۡلِمُ ٱلنَّاسَ شَيۡـٔٗا وَلَٰكِنَّ ٱلنَّاسَ أَنفُسَهُمۡ يَظۡلِمُونَ ﴾
[يُونس: 44]

Ndithudi Mulungu salakwira anthu koma kuti anthu eni ake amadzipondereza okha

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إن الله لا يظلم الناس شيئا ولكن الناس أنفسهم يظلمون, باللغة نيانجا

﴿إن الله لا يظلم الناس شيئا ولكن الناس أنفسهم يظلمون﴾ [يُونس: 44]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithu Allah sachitira anthu choipa chilichonse. Koma anthu akudzichitira okha zoipa. (Adapatsidwa nzeru, koma sazigwiritsa ntchito)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek