×

Iwo amanena kuti: “Mulungu wabereka mwana wamwamuna.” Mulungu ayeretsedwe ndi zimenezo. “Iye 10:68 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:68) ayat 68 in Chichewa

10:68 Surah Yunus ayat 68 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 68 - يُونس - Page - Juz 11

﴿قَالُواْ ٱتَّخَذَ ٱللَّهُ وَلَدٗاۗ سُبۡحَٰنَهُۥۖ هُوَ ٱلۡغَنِيُّۖ لَهُۥ مَا فِي ٱلسَّمَٰوَٰتِ وَمَا فِي ٱلۡأَرۡضِۚ إِنۡ عِندَكُم مِّن سُلۡطَٰنِۭ بِهَٰذَآۚ أَتَقُولُونَ عَلَى ٱللَّهِ مَا لَا تَعۡلَمُونَ ﴾
[يُونس: 68]

Iwo amanena kuti: “Mulungu wabereka mwana wamwamuna.” Mulungu ayeretsedwe ndi zimenezo. “Iye ndi Wolemera. Zake ndi zonse zimene zili m’lengalenga ndi padzikolapansi. Paichiinumulibeumboni. Kodimukunena zinthu zokhudza Mulungu zimene simuzidziwa?”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قالوا اتخذ الله ولدا سبحانه هو الغني له ما في السموات وما, باللغة نيانجا

﴿قالوا اتخذ الله ولدا سبحانه هو الغني له ما في السموات وما﴾ [يُونس: 68]

Khaled Ibrahim Betala
“Akunena: “Allah wadzipangira mwana.” Wapatukana ndi zimenezo! Iye Ngokwanira, (salakalaka mwana ngakhale mthangati aliyense). NdiZake (zonse) za kumwamba ndi za pansi. Inu mulibe umboni pa zimenezi. Kodi mukumnenera Allah zomwe simukuzidziwa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek