×

Kodi padalinso mzinda wina umene unakhulupirira ndipo kuti chikhulupiriro chake chinaupulumutsa kupatula 10:98 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:98) ayat 98 in Chichewa

10:98 Surah Yunus ayat 98 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 98 - يُونس - Page - Juz 11

﴿فَلَوۡلَا كَانَتۡ قَرۡيَةٌ ءَامَنَتۡ فَنَفَعَهَآ إِيمَٰنُهَآ إِلَّا قَوۡمَ يُونُسَ لَمَّآ ءَامَنُواْ كَشَفۡنَا عَنۡهُمۡ عَذَابَ ٱلۡخِزۡيِ فِي ٱلۡحَيَوٰةِ ٱلدُّنۡيَا وَمَتَّعۡنَٰهُمۡ إِلَىٰ حِينٖ ﴾
[يُونس: 98]

Kodi padalinso mzinda wina umene unakhulupirira ndipo kuti chikhulupiriro chake chinaupulumutsa kupatula anthu a Yona, pamene iwo adakhulupirira? Ife tidawachotsera chilango chochititsa manyazi m’moyo uno ndi kuwalola kusangalala pa kanthawi kochepa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فلولا كانت قرية آمنت فنفعها إيمانها إلا قوم يونس لما آمنوا كشفنا, باللغة نيانجا

﴿فلولا كانت قرية آمنت فنفعها إيمانها إلا قوم يونس لما آمنوا كشفنا﴾ [يُونس: 98]

Khaled Ibrahim Betala
“Kodi udalipo mudzi (ndi umodzi womwe pakati pa midzi mwa yomwe tidaiwononga), umene udalapa ndi kukhulupirira (pambuyo poona chilango kotero kuti) chikhulupiliro chake nkuuthandiza pa nthawi imeneyo, osati kupatula anthu a Yunus okha? Pamene adakhulupirira, tidawachotsera chilango choyalutsa m’moyo wa padziko lapansi, ndipo tidawasangalatsa kufikira nthawi yawo (yofera)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek