×

Koma ngati Ife titamuonetsa munthu chisoni chathu, pambuyo pa mavuto amene adapeza, 11:10 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:10) ayat 10 in Chichewa

11:10 Surah Hud ayat 10 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 10 - هُود - Page - Juz 12

﴿وَلَئِنۡ أَذَقۡنَٰهُ نَعۡمَآءَ بَعۡدَ ضَرَّآءَ مَسَّتۡهُ لَيَقُولَنَّ ذَهَبَ ٱلسَّيِّـَٔاتُ عَنِّيٓۚ إِنَّهُۥ لَفَرِحٞ فَخُورٌ ﴾
[هُود: 10]

Koma ngati Ife titamuonetsa munthu chisoni chathu, pambuyo pa mavuto amene adapeza, iye adzati: “Mavuto atha kwa ine” Ndithudi iye amakhala mosalabadira ndiponso modzikweza kwambiri

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولئن أذقناه نعماء بعد ضراء مسته ليقولن ذهب السيئات عني إنه لفرح, باللغة نيانجا

﴿ولئن أذقناه نعماء بعد ضراء مسته ليقولن ذهب السيئات عني إنه لفرح﴾ [هُود: 10]

Khaled Ibrahim Betala
“Koma ngati titamulawitsa mtendere pambuyo pa masautso omwe adamkhudza, amati: “Masautso andichoka,”(ndipo sakhala wotanganidwa ndi ntchito zabwino zosonyeza kuyamika Allah), ndithudi iye amakhala wosangalala, wodzitukumula
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek