×

Ndithudi Ife tidamupatsa Mose Buku koma mikangano inabuka pakati pawo ndipo kukadapanda 11:110 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:110) ayat 110 in Chichewa

11:110 Surah Hud ayat 110 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 110 - هُود - Page - Juz 12

﴿وَلَقَدۡ ءَاتَيۡنَا مُوسَى ٱلۡكِتَٰبَ فَٱخۡتُلِفَ فِيهِۚ وَلَوۡلَا كَلِمَةٞ سَبَقَتۡ مِن رَّبِّكَ لَقُضِيَ بَيۡنَهُمۡۚ وَإِنَّهُمۡ لَفِي شَكّٖ مِّنۡهُ مُرِيبٖ ﴾
[هُود: 110]

Ndithudi Ife tidamupatsa Mose Buku koma mikangano inabuka pakati pawo ndipo kukadapanda kuti liwu lochokera kwa Ambuye wako lidatsogola kale, lamulo likadadza pa iwo. Ndithudi iwo ndi okaika kwambiri za ili

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولقد آتينا موسى الكتاب فاختلف فيه ولولا كلمة سبقت من ربك لقضي, باللغة نيانجا

﴿ولقد آتينا موسى الكتاب فاختلف فيه ولولا كلمة سبقت من ربك لقضي﴾ [هُود: 110]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo ndithu tidampatsa buku Mûsa, koma kusiyana kudabuka mmenemo (pakatanthauzidwe ka bukulo pambuyo pa Mûsa). Pakadapanda mawu a Mbuye wako omwe adatsogola (oti sadzawalanga nthawi isanafike), ndithu kukadaweruzidwa pakati pawo. Ndipo ndithu iwo ali m’kukaika ndi kupeneka (kwakukulu) pa zimenezo
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek