×

Kufikira pamene chilamulo chathu chidadza, ndipo nthaka idayamba kutulutsa madzi. Ife tinati: 11:40 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:40) ayat 40 in Chichewa

11:40 Surah Hud ayat 40 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 40 - هُود - Page - Juz 12

﴿حَتَّىٰٓ إِذَا جَآءَ أَمۡرُنَا وَفَارَ ٱلتَّنُّورُ قُلۡنَا ٱحۡمِلۡ فِيهَا مِن كُلّٖ زَوۡجَيۡنِ ٱثۡنَيۡنِ وَأَهۡلَكَ إِلَّا مَن سَبَقَ عَلَيۡهِ ٱلۡقَوۡلُ وَمَنۡ ءَامَنَۚ وَمَآ ءَامَنَ مَعَهُۥٓ إِلَّا قَلِيلٞ ﴾
[هُود: 40]

Kufikira pamene chilamulo chathu chidadza, ndipo nthaka idayamba kutulutsa madzi. Ife tinati: “Lowetsa m’chombo zinthu ziwiriziwiri, (chachimuna ndi chachikazi), anthu a banja lako kupatula iye amene chiweruzo chaperekedwa kale ndi iwo amene akhulupilira. Koma si ambiri amene adali okhulupirira ndi iye kupatula ochepa okha

❮ Previous Next ❯

ترجمة: حتى إذا جاء أمرنا وفار التنور قلنا احمل فيها من كل زوجين, باللغة نيانجا

﴿حتى إذا جاء أمرنا وفار التنور قلنا احمل فيها من كل زوجين﴾ [هُود: 40]

Khaled Ibrahim Betala
“Kufikira pamene lidadza lamulo lathu, madzi naphulika mu uvuni, (chomwe chidali chisonyezo cha Nuh chosonyeza kudza kwa lamulo loona kwa anthu ake) tidamuuza (kuti): “Kweza m’menemo (m’chombo) mtundu uliwonse (wa nyama), ziwiriziwiri, (yaikazi ndi yaimuna), ndi anthu a kubanja lako kupatula omwe chiweruzo (cha Allah) chatsimikizidwa pa iwo (kuti aonongeke), ndipo (atengenso onse) amene akhulupirira.” Komatu ndi ochepa kwambiri amene adakhulupirira pamodzi ndi iye
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek