×

Nowa adati: “Ine ndipempha chitetezo chanu, Ambuye, chifukwa chokupemphani zinthu zimene ine 11:47 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:47) ayat 47 in Chichewa

11:47 Surah Hud ayat 47 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 47 - هُود - Page - Juz 12

﴿قَالَ رَبِّ إِنِّيٓ أَعُوذُ بِكَ أَنۡ أَسۡـَٔلَكَ مَا لَيۡسَ لِي بِهِۦ عِلۡمٞۖ وَإِلَّا تَغۡفِرۡ لِي وَتَرۡحَمۡنِيٓ أَكُن مِّنَ ٱلۡخَٰسِرِينَ ﴾
[هُود: 47]

Nowa adati: “Ine ndipempha chitetezo chanu, Ambuye, chifukwa chokupemphani zinthu zimene ine sindili kuzidziwa. Ndipo Inu ngati simundikhululukira ndi kundimvera ine chisoni, ndithudi, ine ndidzakhala mmodzi wa anthu olephera.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قال رب إني أعوذ بك أن أسألك ما ليس لي به علم, باللغة نيانجا

﴿قال رب إني أعوذ بك أن أسألك ما ليس لي به علم﴾ [هُود: 47]

Khaled Ibrahim Betala
“(Nuh) adati: “E Mbuye wanga! Ndikudziteteza mwa Inu kuti ndisakupempheninso zomwe sindikuzidziwa. Ngati simundikhululukira ndi kundichitira chifundo, ndikhala mwa anthu otaika.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek