×

“Zimene tilikunena ndizakuti ina ya milungu yathu yakupatsa iwe tsoka.” Iye adati: 11:54 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:54) ayat 54 in Chichewa

11:54 Surah Hud ayat 54 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 54 - هُود - Page - Juz 12

﴿إِن نَّقُولُ إِلَّا ٱعۡتَرَىٰكَ بَعۡضُ ءَالِهَتِنَا بِسُوٓءٖۗ قَالَ إِنِّيٓ أُشۡهِدُ ٱللَّهَ وَٱشۡهَدُوٓاْ أَنِّي بَرِيٓءٞ مِّمَّا تُشۡرِكُونَ ﴾
[هُود: 54]

“Zimene tilikunena ndizakuti ina ya milungu yathu yakupatsa iwe tsoka.” Iye adati: “Ndithudi Mulungu ndiye mboni yanga ndipo nanunso chitirani umboni kuti ine ndatalikirana nazo zimene mukamapembedza mulikuonjezera.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إن نقول إلا اعتراك بعض آلهتنا بسوء قال إني أشهد الله واشهدوا, باللغة نيانجا

﴿إن نقول إلا اعتراك بعض آلهتنا بسوء قال إني أشهد الله واشهدوا﴾ [هُود: 54]

Khaled Ibrahim Betala
““Sitinena kanthu, koma kuti (mwina) milungu yathu ina yakulodza misala.” (Iye) adati: “Ndithu ine ndikupereka umboni kwa Allah ndipo inunso perekani umboni kuti ine ndili kutali ndi zimene mukumphatikiza nazo (Allah pomazipembedza).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek