×

“Ndipo ngati mutembenuka, ine ndakuuzani Uthenga umene ndatumizidwa kwa inu. Ambuye wanga 11:57 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:57) ayat 57 in Chichewa

11:57 Surah Hud ayat 57 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 57 - هُود - Page - Juz 12

﴿فَإِن تَوَلَّوۡاْ فَقَدۡ أَبۡلَغۡتُكُم مَّآ أُرۡسِلۡتُ بِهِۦٓ إِلَيۡكُمۡۚ وَيَسۡتَخۡلِفُ رَبِّي قَوۡمًا غَيۡرَكُمۡ وَلَا تَضُرُّونَهُۥ شَيۡـًٔاۚ إِنَّ رَبِّي عَلَىٰ كُلِّ شَيۡءٍ حَفِيظٞ ﴾
[هُود: 57]

“Ndipo ngati mutembenuka, ine ndakuuzani Uthenga umene ndatumizidwa kwa inu. Ambuye wanga adzaika, m’malo mwanu, anthu ena ndipo inu simungamuchite chinthu choipa chilichonse. Ndithudi Ambuye wanga ndi Msungi wa zinthu zonse.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فإن تولوا فقد أبلغتكم ما أرسلت به إليكم ويستخلف ربي قوما غيركم, باللغة نيانجا

﴿فإن تولوا فقد أبلغتكم ما أرسلت به إليكم ويستخلف ربي قوما غيركم﴾ [هُود: 57]

Khaled Ibrahim Betala
““Ngati munyoza (kulandira chimene ndakuuzani palibe vuto kwa ine); ndithu ndafikitsa kwa inu chimene ndatumidwa. Ndipo Mbuye wanga (awaononga osakhulupirira, ndipo) abweretsa anthu ena m’malo mwanu, ndipo inu simungamusautse konse. Ndithu Mbuye wanga ndi Msungi wa chilichonse.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek