×

“Ine ndaika chikhulupiliro changa mwa Mulungu, Ambuye wanga ndiponso Ambuye wanu. Palibe 11:56 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:56) ayat 56 in Chichewa

11:56 Surah Hud ayat 56 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 56 - هُود - Page - Juz 12

﴿إِنِّي تَوَكَّلۡتُ عَلَى ٱللَّهِ رَبِّي وَرَبِّكُمۚ مَّا مِن دَآبَّةٍ إِلَّا هُوَ ءَاخِذُۢ بِنَاصِيَتِهَآۚ إِنَّ رَبِّي عَلَىٰ صِرَٰطٖ مُّسۡتَقِيمٖ ﴾
[هُود: 56]

“Ine ndaika chikhulupiliro changa mwa Mulungu, Ambuye wanga ndiponso Ambuye wanu. Palibe chinthu cha moyo pa dziko lapansi chimene tsogolo lake sililamulidwa ndi Iye. Ndithudi Ambuye wanga ndi amene ali pa njira yoyenera.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إني توكلت على الله ربي وربكم ما من دابة إلا هو آخذ, باللغة نيانجا

﴿إني توكلت على الله ربي وربكم ما من دابة إلا هو آخذ﴾ [هُود: 56]

Khaled Ibrahim Betala
““Ndithu ine ndatsamira kwa Allah, Mbuye wanga yemwenso ali Mbuye wanu. Palibe chinyama chilichonse koma Allah wachigwira tsumba lake (ndikuchiyendetsa mmene akufunira). Ndithudi, Mbuye wanga Ngwachilungamo.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek