×

Iye adati: “Ine ndikadakhala ndi mphamvu zoti ndikugonjetseni kapena ndikanapeza munthu wina 11:80 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:80) ayat 80 in Chichewa

11:80 Surah Hud ayat 80 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 80 - هُود - Page - Juz 12

﴿قَالَ لَوۡ أَنَّ لِي بِكُمۡ قُوَّةً أَوۡ ءَاوِيٓ إِلَىٰ رُكۡنٖ شَدِيدٖ ﴾
[هُود: 80]

Iye adati: “Ine ndikadakhala ndi mphamvu zoti ndikugonjetseni kapena ndikanapeza munthu wina wamphamvu zambiri ndikadamenyana nanu.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قال لو أن لي بكم قوة أو آوي إلى ركن شديد, باللغة نيانجا

﴿قال لو أن لي بكم قوة أو آوي إلى ركن شديد﴾ [هُود: 80]

Khaled Ibrahim Betala
“(Iye) adati: “Ndikadakhala nayo mphamvu (yomenyana nanu) kapena kotsamira kolimba kwamphamvu (ndikadalimbana nanu kuti musachite zauve ndi alendowa).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek