×

“Ine ndidatsatira chipembedzo cha makolo anga, Abrahamu, Isake ndi Yakobo. Sikuli koyenera 12:38 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yusuf ⮕ (12:38) ayat 38 in Chichewa

12:38 Surah Yusuf ayat 38 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yusuf ayat 38 - يُوسُف - Page - Juz 12

﴿وَٱتَّبَعۡتُ مِلَّةَ ءَابَآءِيٓ إِبۡرَٰهِيمَ وَإِسۡحَٰقَ وَيَعۡقُوبَۚ مَا كَانَ لَنَآ أَن نُّشۡرِكَ بِٱللَّهِ مِن شَيۡءٖۚ ذَٰلِكَ مِن فَضۡلِ ٱللَّهِ عَلَيۡنَا وَعَلَى ٱلنَّاسِ وَلَٰكِنَّ أَكۡثَرَ ٱلنَّاسِ لَا يَشۡكُرُونَ ﴾
[يُوسُف: 38]

“Ine ndidatsatira chipembedzo cha makolo anga, Abrahamu, Isake ndi Yakobo. Sikuli koyenera kwa ife kum’phatikiza Mulungu ndi chilichonse. Ichi ndi chisomo cha Mulungu kwa ife ndi kwa anthu a mitundu yonse, koma anthu ambiri sayamika ayi.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: واتبعت ملة آبائي إبراهيم وإسحاق ويعقوب ما كان لنا أن نشرك بالله, باللغة نيانجا

﴿واتبعت ملة آبائي إبراهيم وإسحاق ويعقوب ما كان لنا أن نشرك بالله﴾ [يُوسُف: 38]

Khaled Ibrahim Betala
““Ndipo ine ndatsata chipembedzo cha makolo anga Ibrahim, Ishâq ndi Ya’qub; ndipo sikudali koyenera kwa ife kumphatikiza Allah ndi chilichonse. (Ndipo kuzindikira) zimenezi ndi ubwino wa Allah umene uli pa ife ndi anthu ena, koma anthu ambiri sathokoza.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek