×

Mfumu idati, “Mubweretseni iye kwa ine kuti ndimusankhe iye kukhala munthu wanga.” 12:54 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yusuf ⮕ (12:54) ayat 54 in Chichewa

12:54 Surah Yusuf ayat 54 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yusuf ayat 54 - يُوسُف - Page - Juz 13

﴿وَقَالَ ٱلۡمَلِكُ ٱئۡتُونِي بِهِۦٓ أَسۡتَخۡلِصۡهُ لِنَفۡسِيۖ فَلَمَّا كَلَّمَهُۥ قَالَ إِنَّكَ ٱلۡيَوۡمَ لَدَيۡنَا مَكِينٌ أَمِينٞ ﴾
[يُوسُف: 54]

Mfumu idati, “Mubweretseni iye kwa ine kuti ndimusankhe iye kukhala munthu wanga.” Ndipo atayankhula naye, Mfumu idati, “Ndithudi iwe udzakhala ndi ife kuyambira lero ndipo udzakhala wolemekezeka ndiponso wokhulupirika.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وقال الملك ائتوني به أستخلصه لنفسي فلما كلمه قال إنك اليوم لدينا, باللغة نيانجا

﴿وقال الملك ائتوني به أستخلصه لنفسي فلما كلمه قال إنك اليوم لدينا﴾ [يُوسُف: 54]

Khaled Ibrahim Betala
“Choncho Mfumu idati: “Mubwere naye kwa ine kuti ine mwini ndimsankhe.” Ndipo pamene adayankhula naye, (Mfumu) idati: “Ndithu iwe lero kwa ife wakhala wolemekezeka, wokhulupirika.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek