×

Mulungu ndi amene adakweza mlengalenga popanda nsanamira yomwe mungaione. Ndipo Iye adabuka 13:2 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ar-Ra‘d ⮕ (13:2) ayat 2 in Chichewa

13:2 Surah Ar-Ra‘d ayat 2 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ar-Ra‘d ayat 2 - الرَّعد - Page - Juz 13

﴿ٱللَّهُ ٱلَّذِي رَفَعَ ٱلسَّمَٰوَٰتِ بِغَيۡرِ عَمَدٖ تَرَوۡنَهَاۖ ثُمَّ ٱسۡتَوَىٰ عَلَى ٱلۡعَرۡشِۖ وَسَخَّرَ ٱلشَّمۡسَ وَٱلۡقَمَرَۖ كُلّٞ يَجۡرِي لِأَجَلٖ مُّسَمّٗىۚ يُدَبِّرُ ٱلۡأَمۡرَ يُفَصِّلُ ٱلۡأٓيَٰتِ لَعَلَّكُم بِلِقَآءِ رَبِّكُمۡ تُوقِنُونَ ﴾
[الرَّعد: 2]

Mulungu ndi amene adakweza mlengalenga popanda nsanamira yomwe mungaione. Ndipo Iye adabuka pamwamba pa Mpando wa Chifumu ndipo adalamulira dzuwa ndi mwezi, ndipo chilichonse chimayenda monga momwe chidalamulidwira kufikira munthawi yake. Iye amalamulira zinthu zonse ndipo amafotokoza chivumbulutso chake momveka kuti inu mukhulupirire zoti mudzakumana ndi Ambuye wanu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: الله الذي رفع السموات بغير عمد ترونها ثم استوى على العرش وسخر, باللغة نيانجا

﴿الله الذي رفع السموات بغير عمد ترونها ثم استوى على العرش وسخر﴾ [الرَّعد: 2]

Khaled Ibrahim Betala
“Allah ndi Yemwe adatukula thambo popanda mizati imene mukuiona; kenako adakhazikika pa Arsh (Mpando Wachifumu Waukulu, kukhazikika koyenera ndi Iye komwe kulibe chofanizira); ndipo adafewetsa dzuwa ndi mwezi (kwa anthu). Chilichonse mwa zimenezi chikupitilira kuyenda mpaka nyengo imene idaikidwa. Iye ndi Yemwe akuyendetsa zinthu; akulongosola Ayah (ndime) kuti mukhale ndi chitsimikizo pa zakukumana ndi Mbuye wanu
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek