×

Iwoameneamaphwanyalonjezola Mulunguatalilandira ndipo amalekanitsa zinthu zimene Iye adawalamulira kuti azilumikize, ndipo amachita 13:25 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ar-Ra‘d ⮕ (13:25) ayat 25 in Chichewa

13:25 Surah Ar-Ra‘d ayat 25 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ar-Ra‘d ayat 25 - الرَّعد - Page - Juz 13

﴿وَٱلَّذِينَ يَنقُضُونَ عَهۡدَ ٱللَّهِ مِنۢ بَعۡدِ مِيثَٰقِهِۦ وَيَقۡطَعُونَ مَآ أَمَرَ ٱللَّهُ بِهِۦٓ أَن يُوصَلَ وَيُفۡسِدُونَ فِي ٱلۡأَرۡضِ أُوْلَٰٓئِكَ لَهُمُ ٱللَّعۡنَةُ وَلَهُمۡ سُوٓءُ ٱلدَّارِ ﴾
[الرَّعد: 25]

Iwoameneamaphwanyalonjezola Mulunguatalilandira ndipo amalekanitsa zinthu zimene Iye adawalamulira kuti azilumikize, ndipo amachita zinthu zoipa pa dziko lapansi, temberero lidzaikidwa pa iwo ndipo malo awo okhala adzakhala osasangalatsa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: والذين ينقضون عهد الله من بعد ميثاقه ويقطعون ما أمر الله به, باللغة نيانجا

﴿والذين ينقضون عهد الله من بعد ميثاقه ويقطعون ما أمر الله به﴾ [الرَّعد: 25]

Khaled Ibrahim Betala
“Koma amene akuswa lonjezo la Allah (ndi malonjezo a anthu anzawo) pambuyo polimanga motsimikiza, ndi kumadula chimene Allah walamula kuti chilumikizidwe, ndi kumaononga padziko, iwowo ndiwo adzapeza tembelero; ndiponso adzapeza Nyumba yoipa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek