×

Chitsanzo cha Paradiso imene anthu oopa Mulungu adalonjezedwa, pansi pake pamadutsa mitsinje; 13:35 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ar-Ra‘d ⮕ (13:35) ayat 35 in Chichewa

13:35 Surah Ar-Ra‘d ayat 35 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ar-Ra‘d ayat 35 - الرَّعد - Page - Juz 13

﴿۞ مَّثَلُ ٱلۡجَنَّةِ ٱلَّتِي وُعِدَ ٱلۡمُتَّقُونَۖ تَجۡرِي مِن تَحۡتِهَا ٱلۡأَنۡهَٰرُۖ أُكُلُهَا دَآئِمٞ وَظِلُّهَاۚ تِلۡكَ عُقۡبَى ٱلَّذِينَ ٱتَّقَواْۚ وَّعُقۡبَى ٱلۡكَٰفِرِينَ ٱلنَّارُ ﴾
[الرَّعد: 35]

Chitsanzo cha Paradiso imene anthu oopa Mulungu adalonjezedwa, pansi pake pamadutsa mitsinje; zipatso zake ndi zosatha ndi mithunzi yake ndi yosathanso. Imeneyi ndiyo mphotho ya anthu oopa Mulungu. Koma mphotho ya anthu osakhulupirira ndi moto

❮ Previous Next ❯

ترجمة: مثل الجنة التي وعد المتقون تجري من تحتها الأنهار أكلها دائم وظلها, باللغة نيانجا

﴿مثل الجنة التي وعد المتقون تجري من تحتها الأنهار أكلها دائم وظلها﴾ [الرَّعد: 35]

Khaled Ibrahim Betala
“Fanizo la Munda wamtendere umene alonjezedwa amene akuopa Allah (uli tere:) Pansi (ndi patsogolo) pake ikuyenda mitsinje. Zipatso zake ndi mthunzi wake nzanthawi zonse. Awa ndiwo malekezero a omwe akuopa Allah; koma malekezero a osakhulupirira ndi ku Moto basi
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek