×

Ndithudi iwo amene adalipo awa asanadze nawonso adali kuchita ziwembu koma chikonzero 13:42 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ar-Ra‘d ⮕ (13:42) ayat 42 in Chichewa

13:42 Surah Ar-Ra‘d ayat 42 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ar-Ra‘d ayat 42 - الرَّعد - Page - Juz 13

﴿وَقَدۡ مَكَرَ ٱلَّذِينَ مِن قَبۡلِهِمۡ فَلِلَّهِ ٱلۡمَكۡرُ جَمِيعٗاۖ يَعۡلَمُ مَا تَكۡسِبُ كُلُّ نَفۡسٖۗ وَسَيَعۡلَمُ ٱلۡكُفَّٰرُ لِمَنۡ عُقۡبَى ٱلدَّارِ ﴾
[الرَّعد: 42]

Ndithudi iwo amene adalipo awa asanadze nawonso adali kuchita ziwembu koma chikonzero chonse ndi cha Mulungu. Iye amadziwa chimene aliyense amalandira ndipo anthu osakhulupirira adzadziwa kuti kodi ndani amene adzalandira ubwino pomaliza

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وقد مكر الذين من قبلهم فلله المكر جميعا يعلم ما تكسب كل, باللغة نيانجا

﴿وقد مكر الذين من قبلهم فلله المكر جميعا يعلم ما تكسب كل﴾ [الرَّعد: 42]

Khaled Ibrahim Betala
“Koma amene adalipo kale iwo kulibe, adachita ziwembu; koma kuononga ziwembu zonsezo nkwa Allah basi. (Iye) akudziwa zimene cholengedwa chilichonse chachita. Ndipo osakhulupirira adzadziwa zotsatira zabwino za Nyumba ya tsiku la chimaliziro kuti zidzakhala zayani
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek