×

Iwo ameneamakondamoyounokuposamoyoumeneulinkudza ndipo amaletsa kutsatira njira ya Mulungu ndipo amafuna za chinyengo 14:3 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ibrahim ⮕ (14:3) ayat 3 in Chichewa

14:3 Surah Ibrahim ayat 3 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ibrahim ayat 3 - إبراهِيم - Page - Juz 13

﴿ٱلَّذِينَ يَسۡتَحِبُّونَ ٱلۡحَيَوٰةَ ٱلدُّنۡيَا عَلَى ٱلۡأٓخِرَةِ وَيَصُدُّونَ عَن سَبِيلِ ٱللَّهِ وَيَبۡغُونَهَا عِوَجًاۚ أُوْلَٰٓئِكَ فِي ضَلَٰلِۭ بَعِيدٖ ﴾
[إبراهِيم: 3]

Iwo ameneamakondamoyounokuposamoyoumeneulinkudza ndipo amaletsa kutsatira njira ya Mulungu ndipo amafuna za chinyengo mu izo, iwo ndi wosochera kwambiri

❮ Previous Next ❯

ترجمة: الذين يستحبون الحياة الدنيا على الآخرة ويصدون عن سبيل الله ويبغونها عوجا, باللغة نيانجا

﴿الذين يستحبون الحياة الدنيا على الآخرة ويصدون عن سبيل الله ويبغونها عوجا﴾ [إبراهِيم: 3]

Khaled Ibrahim Betala
“Amene akukondetsa moyo wadziko lapansi kuposa moyo wa pambuyo pa imfa, ndipo amatsekereza (anthu) ku njira ya Allah ndikufuna kuikhotetsa (pomwe njirayo njosakhota). Iwo ali mkusokera kotalikana kwambiri (ndi choonadi)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek