×

Pamene iwo adadza kwa iye ndi kumuuza kuti, “Mtendere ukhale kwa iwe.’ 15:52 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hijr ⮕ (15:52) ayat 52 in Chichewa

15:52 Surah Al-hijr ayat 52 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hijr ayat 52 - الحِجر - Page - Juz 14

﴿إِذۡ دَخَلُواْ عَلَيۡهِ فَقَالُواْ سَلَٰمٗا قَالَ إِنَّا مِنكُمۡ وَجِلُونَ ﴾
[الحِجر: 52]

Pamene iwo adadza kwa iye ndi kumuuza kuti, “Mtendere ukhale kwa iwe.’ Koma iye adawayankha kuti, “Ndili ndi mantha ndi inu.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إذ دخلوا عليه فقالوا سلاما قال إنا منكم وجلون, باللغة نيانجا

﴿إذ دخلوا عليه فقالوا سلاما قال إنا منكم وجلون﴾ [الحِجر: 52]

Khaled Ibrahim Betala
“Pamene adalowa kwa iye ndikunena: “Salaman (Mtendere!)” (Iyenso adawayankha: “Mtendere ukhalenso pa inu.” Ndipo Pamene adaona kuti akana chakudya) Adati: “Ndithu ife tikukuopani.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek