×

Ndipo pamene tidakuuza kuti, “Ndithudi! Ambuye wako wawazungulira anthu. Ndipo Ife sitidapange 17:60 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Isra’ ⮕ (17:60) ayat 60 in Chichewa

17:60 Surah Al-Isra’ ayat 60 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Isra’ ayat 60 - الإسرَاء - Page - Juz 15

﴿وَإِذۡ قُلۡنَا لَكَ إِنَّ رَبَّكَ أَحَاطَ بِٱلنَّاسِۚ وَمَا جَعَلۡنَا ٱلرُّءۡيَا ٱلَّتِيٓ أَرَيۡنَٰكَ إِلَّا فِتۡنَةٗ لِّلنَّاسِ وَٱلشَّجَرَةَ ٱلۡمَلۡعُونَةَ فِي ٱلۡقُرۡءَانِۚ وَنُخَوِّفُهُمۡ فَمَا يَزِيدُهُمۡ إِلَّا طُغۡيَٰنٗا كَبِيرٗا ﴾
[الإسرَاء: 60]

Ndipo pamene tidakuuza kuti, “Ndithudi! Ambuye wako wawazungulira anthu. Ndipo Ife sitidapange masomphenya amene tidakuonetsa iwe koma kukhala mayeso kwa anthu chimodzimodzinso mtengo wotembereredwa umene watchulidwa m’Korani. Ife timawachenjeza ndi kuwachititsa mantha koma sizili kuwathandiza koma kuonjezera kusakhulupirira.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإذ قلنا لك إن ربك أحاط بالناس وما جعلنا الرؤيا التي أريناك, باللغة نيانجا

﴿وإذ قلنا لك إن ربك أحاط بالناس وما جعلنا الرؤيا التي أريناك﴾ [الإسرَاء: 60]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo (kumbuka) pamene tidakuuza kuti ndithu Mbuye wako wawazungulira anthu (mowadziwa bwinobwino;) ndipo sitidawachite maloto omwe tidakuonetsa koma kuti akhale mayeso kwa anthu, (kuti kodi akhulupirira kapena sakhulupirira), ndiponso (kutchula kwa) rntengo wotembeleredwa m’Qur’an (ndimayetseronso kwa iwo;) ndipo tikuwachenjeza, koma (machenjezo athu) sakuwaonjezera china koma kulumpha malire kwakukulu basi
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek