×

Nena, “Ine ndine munthu monga inu nomwe, koma zavumbulutsidwa kwa ine kuti 18:110 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Kahf ⮕ (18:110) ayat 110 in Chichewa

18:110 Surah Al-Kahf ayat 110 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Kahf ayat 110 - الكَهف - Page - Juz 16

﴿قُلۡ إِنَّمَآ أَنَا۠ بَشَرٞ مِّثۡلُكُمۡ يُوحَىٰٓ إِلَيَّ أَنَّمَآ إِلَٰهُكُمۡ إِلَٰهٞ وَٰحِدٞۖ فَمَن كَانَ يَرۡجُواْ لِقَآءَ رَبِّهِۦ فَلۡيَعۡمَلۡ عَمَلٗا صَٰلِحٗا وَلَا يُشۡرِكۡ بِعِبَادَةِ رَبِّهِۦٓ أَحَدَۢا ﴾
[الكَهف: 110]

Nena, “Ine ndine munthu monga inu nomwe, koma zavumbulutsidwa kwa ine kuti Mulungu wanu ndi mmodzi. Kotero aliyense amene afuna kudzakumana ndi Ambuye wake ayenera kuchita zimene zili zabwino ndipo popembedza Ambuye wake, osaphatikizamo wina wake.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قل إنما أنا بشر مثلكم يوحى إلي أنما إلهكم إله واحد فمن, باللغة نيانجا

﴿قل إنما أنا بشر مثلكم يوحى إلي أنما إلهكم إله واحد فمن﴾ [الكَهف: 110]

Khaled Ibrahim Betala
“Nena: “Ndithu ine ndi munthu monga inu, (chosiyana nchakuti) ine ndikupatsidwa chivumbulutso (chonena kuti) ndithu Mulungu wanu ndi Mulungu mmodzi Yekha. Ndipo amene afuna kukumana ndi Mbuye wake, achite zochita zabwino ndipo asaphatikizepo aliyense pa mapemphero a Mbuye wake.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek