×

“Chifukwa ngati iwo adzadziwa za inu, adzakuponyani miyala kapena adzakubwezerani ku chipembedzo 18:20 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Kahf ⮕ (18:20) ayat 20 in Chichewa

18:20 Surah Al-Kahf ayat 20 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Kahf ayat 20 - الكَهف - Page - Juz 15

﴿إِنَّهُمۡ إِن يَظۡهَرُواْ عَلَيۡكُمۡ يَرۡجُمُوكُمۡ أَوۡ يُعِيدُوكُمۡ فِي مِلَّتِهِمۡ وَلَن تُفۡلِحُوٓاْ إِذًا أَبَدٗا ﴾
[الكَهف: 20]

“Chifukwa ngati iwo adzadziwa za inu, adzakuponyani miyala kapena adzakubwezerani ku chipembedzo chawo. Ndipo zitatero inu simudzapambana ayi.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إنهم إن يظهروا عليكم يرجموكم أو يعيدوكم في ملتهم ولن تفلحوا إذا, باللغة نيانجا

﴿إنهم إن يظهروا عليكم يرجموكم أو يعيدوكم في ملتهم ولن تفلحوا إذا﴾ [الكَهف: 20]

Khaled Ibrahim Betala
““Ndithu iwo akakudziwani (pamene mulipa), akugendani ndi miyala; apo ai akubwezerani ku chipeinbedzo chawo (chopotoka), zikatero ndiye kuti simudzapambananso mpaka kalekale.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek