×

Bwanji pamene iwe umalowa m’munda mwako, siudanene kuti, “Izi ndi zimene Mulungu 18:39 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Kahf ⮕ (18:39) ayat 39 in Chichewa

18:39 Surah Al-Kahf ayat 39 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Kahf ayat 39 - الكَهف - Page - Juz 15

﴿وَلَوۡلَآ إِذۡ دَخَلۡتَ جَنَّتَكَ قُلۡتَ مَا شَآءَ ٱللَّهُ لَا قُوَّةَ إِلَّا بِٱللَّهِۚ إِن تَرَنِ أَنَا۠ أَقَلَّ مِنكَ مَالٗا وَوَلَدٗا ﴾
[الكَهف: 39]

Bwanji pamene iwe umalowa m’munda mwako, siudanene kuti, “Izi ndi zimene Mulungu wafuna ndipo kulibe mphamvu kwina kulikonse kupatula kwa Mulungu? Ngakhale iwe ukundiona ine kuti ndine wochepekedwa kwambiri m’chuma ndi ana.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولولا إذ دخلت جنتك قلت ما شاء الله لا قوة إلا بالله, باللغة نيانجا

﴿ولولا إذ دخلت جنتك قلت ما شاء الله لا قوة إلا بالله﴾ [الكَهف: 39]

Khaled Ibrahim Betala
““Ndipo pamene umalowa m’munda wako ukadanena kuti izi ndi zimene wandifunira Allah, mphamvu sizikadapezeka koma kupyolera mwa Allah (zikadakhala zabwino kwa iwe). Ngati ukundiona ine kuti ndili ndi chuma chochepa ndi ana ochepa kuposa iwe (koma sindisiya kutamanda Allah).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek