×

Uwapatse chitsanzo cha moyo wa padziko lapansi. Moyowu uli ngati madzi amene 18:45 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Kahf ⮕ (18:45) ayat 45 in Chichewa

18:45 Surah Al-Kahf ayat 45 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Kahf ayat 45 - الكَهف - Page - Juz 15

﴿وَٱضۡرِبۡ لَهُم مَّثَلَ ٱلۡحَيَوٰةِ ٱلدُّنۡيَا كَمَآءٍ أَنزَلۡنَٰهُ مِنَ ٱلسَّمَآءِ فَٱخۡتَلَطَ بِهِۦ نَبَاتُ ٱلۡأَرۡضِ فَأَصۡبَحَ هَشِيمٗا تَذۡرُوهُ ٱلرِّيَٰحُۗ وَكَانَ ٱللَّهُ عَلَىٰ كُلِّ شَيۡءٖ مُّقۡتَدِرًا ﴾
[الكَهف: 45]

Uwapatse chitsanzo cha moyo wa padziko lapansi. Moyowu uli ngati madzi amene timatsitsa kumwamba ndi mbeu za padziko la pansi zimene zimasakanizana ndi iwo ndipo zimakhala zanthete ndi zobiliwira. Koma pambuyo pake zimauma ndi kufumbutuka ndipo mphepo imazimwaza. Ndipo Mulungu ali ndi mphamvu pa chilichonse

❮ Previous Next ❯

ترجمة: واضرب لهم مثل الحياة الدنيا كماء أنـزلناه من السماء فاختلط به نبات, باللغة نيانجا

﴿واضرب لهم مثل الحياة الدنيا كماء أنـزلناه من السماء فاختلط به نبات﴾ [الكَهف: 45]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo apatse fanizo la moyo wadziko lapansi, uli ngati madzi amene tikutsitsa kuchokera kumitambo kenako (madziwo) amasakanikirana ndi mmera wa m’nthaka (ndikuyamba kumera mokongola), kenako (mmerawo) nkukhala masamba ouma odukaduka omwe mphepo ikuwaulutsa uku ndi uku. Ndipo Allah ali ndi mphamvu pachilichonse
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek