×

Koma magulu a Akhirisitu adasemphana maganizo pakati pawo. Koma pamene tsiku loopsa 19:37 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Maryam ⮕ (19:37) ayat 37 in Chichewa

19:37 Surah Maryam ayat 37 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Maryam ayat 37 - مَريَم - Page - Juz 16

﴿فَٱخۡتَلَفَ ٱلۡأَحۡزَابُ مِنۢ بَيۡنِهِمۡۖ فَوَيۡلٞ لِّلَّذِينَ كَفَرُواْ مِن مَّشۡهَدِ يَوۡمٍ عَظِيمٍ ﴾
[مَريَم: 37]

Koma magulu a Akhirisitu adasemphana maganizo pakati pawo. Koma pamene tsiku loopsa lidza, tsoka kwa anthu osakhulupirira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فاختلف الأحزاب من بينهم فويل للذين كفروا من مشهد يوم عظيم, باللغة نيانجا

﴿فاختلف الأحزاب من بينهم فويل للذين كفروا من مشهد يوم عظيم﴾ [مَريَم: 37]

Khaled Ibrahim Betala
“Koma magulu (a Akhrisitu ndi Ayuda) adapatukana pakati pawo; (ena adamuyesa Isa (Yesu) kuti ndimwana wa Mulungu, ndipo ena adamuyesa Mulungu weniweni, pomwe Ayuda ankati ndi mwana wobadwa m’njira ya chiwerewere), choncho chilango chaukali chidzatsimikizika pa amene sadakhulupirire pokaonekera tsiku lalikululo (kwa Allah)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek