×

Abrahamu adati, “Mtendere ukhale kwa inu. Ine ndidzapempha Ambuye wanga kuti akukhululukireni 19:47 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Maryam ⮕ (19:47) ayat 47 in Chichewa

19:47 Surah Maryam ayat 47 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Maryam ayat 47 - مَريَم - Page - Juz 16

﴿قَالَ سَلَٰمٌ عَلَيۡكَۖ سَأَسۡتَغۡفِرُ لَكَ رَبِّيٓۖ إِنَّهُۥ كَانَ بِي حَفِيّٗا ﴾
[مَريَم: 47]

Abrahamu adati, “Mtendere ukhale kwa inu. Ine ndidzapempha Ambuye wanga kuti akukhululukireni popeza, Mulungu, kwa ine, ndi wokoma mtima.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قال سلام عليك سأستغفر لك ربي إنه كان بي حفيا, باللغة نيانجا

﴿قال سلام عليك سأستغفر لك ربي إنه كان بي حفيا﴾ [مَريَم: 47]

Khaled Ibrahim Betala
“(Ibrahim) adati: “Mtendere ukhale pa inu! Ndikupempherani chikhululuko kwa Mbuye wanga (ngakhale mwandipirikitsa). Ndithu iye amandichitira chisoni kwambiri.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek