×

Ndipo lamulira banja lako kupemphera ndipo ukhale wopirira pokwaniritsa mapemphero. Ife sitipempha 20:132 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ta-Ha ⮕ (20:132) ayat 132 in Chichewa

20:132 Surah Ta-Ha ayat 132 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ta-Ha ayat 132 - طه - Page - Juz 16

﴿وَأۡمُرۡ أَهۡلَكَ بِٱلصَّلَوٰةِ وَٱصۡطَبِرۡ عَلَيۡهَاۖ لَا نَسۡـَٔلُكَ رِزۡقٗاۖ نَّحۡنُ نَرۡزُقُكَۗ وَٱلۡعَٰقِبَةُ لِلتَّقۡوَىٰ ﴾
[طه: 132]

Ndipo lamulira banja lako kupemphera ndipo ukhale wopirira pokwaniritsa mapemphero. Ife sitipempha zinthu kwa iwe koma Ife timakupatsa zofuna zako. Ndipo mapeto abwino ndi a anthu oopa Mulungu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وأمر أهلك بالصلاة واصطبر عليها لا نسألك رزقا نحن نرزقك والعاقبة للتقوى, باللغة نيانجا

﴿وأمر أهلك بالصلاة واصطبر عليها لا نسألك رزقا نحن نرزقك والعاقبة للتقوى﴾ [طه: 132]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo lamula banja lako kupemphera Swala ndi kuipirira iwe mwini Swalayo. Sitikukupempha rizq, (chakudya) koma Ife ndi amene tikukudyetsa ndipo malekezero abwino ali mukuopa (Allah)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek