×

Ndithudi Ife tidamuuza Mose kuti, “Nyamuka nthawi yausiku pamodzi ndi akapolo anga 20:77 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ta-Ha ⮕ (20:77) ayat 77 in Chichewa

20:77 Surah Ta-Ha ayat 77 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ta-Ha ayat 77 - طه - Page - Juz 16

﴿وَلَقَدۡ أَوۡحَيۡنَآ إِلَىٰ مُوسَىٰٓ أَنۡ أَسۡرِ بِعِبَادِي فَٱضۡرِبۡ لَهُمۡ طَرِيقٗا فِي ٱلۡبَحۡرِ يَبَسٗا لَّا تَخَٰفُ دَرَكٗا وَلَا تَخۡشَىٰ ﴾
[طه: 77]

Ndithudi Ife tidamuuza Mose kuti, “Nyamuka nthawi yausiku pamodzi ndi akapolo anga ndipo uwatsekulire njira pakati pa nyanja ndipo usaope kuti akupeza, kapena kumira m’nyanja.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولقد أوحينا إلى موسى أن أسر بعبادي فاضرب لهم طريقا في البحر, باللغة نيانجا

﴿ولقد أوحينا إلى موسى أن أسر بعبادي فاضرب لهم طريقا في البحر﴾ [طه: 77]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo ndithu Mûsa tidamtumizira chivumbulutso, (tidamzindikiritsa kuti): “Yenda usiku ndi akapolo Anga (kutuluka m’dziko la Iguputo,) ndipo ukawapangire panyanja njira youma, ndipo usaope kukupeza adani ndiponso usaope (kumira).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek