×

Ndipo, ndithudi, Ine ndimakhululukira aliyense amene alapa, akhulupirira ndipo achita ntchito zabwino 20:82 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ta-Ha ⮕ (20:82) ayat 82 in Chichewa

20:82 Surah Ta-Ha ayat 82 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ta-Ha ayat 82 - طه - Page - Juz 16

﴿وَإِنِّي لَغَفَّارٞ لِّمَن تَابَ وَءَامَنَ وَعَمِلَ صَٰلِحٗا ثُمَّ ٱهۡتَدَىٰ ﴾
[طه: 82]

Ndipo, ndithudi, Ine ndimakhululukira aliyense amene alapa, akhulupirira ndipo achita ntchito zabwino ndiponso apitiriza kuzichita

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإني لغفار لمن تاب وآمن وعمل صالحا ثم اهتدى, باللغة نيانجا

﴿وإني لغفار لمن تاب وآمن وعمل صالحا ثم اهتدى﴾ [طه: 82]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo ndithu Ine ndi Wokhululuka kwambiri kwa amene walapa ndi kukhulupirira, ndikuchita ntchito zabwino, kenako ndikutsata chiongoko mwaubwino
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek