×

Ndipo iye adawatulutsira iwo chifanizo cha thupi la ng’ombe chimene chidali ndi 20:88 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ta-Ha ⮕ (20:88) ayat 88 in Chichewa

20:88 Surah Ta-Ha ayat 88 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ta-Ha ayat 88 - طه - Page - Juz 16

﴿فَأَخۡرَجَ لَهُمۡ عِجۡلٗا جَسَدٗا لَّهُۥ خُوَارٞ فَقَالُواْ هَٰذَآ إِلَٰهُكُمۡ وَإِلَٰهُ مُوسَىٰ فَنَسِيَ ﴾
[طه: 88]

Ndipo iye adawatulutsira iwo chifanizo cha thupi la ng’ombe chimene chidali ndi mawu. Iwo adati, “Uyu ndi mulungu wanu ndi mulungu wa Mose yemwe adamuiwala.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فأخرج لهم عجلا جسدا له خوار فقالوا هذا إلهكم وإله موسى فنسي, باللغة نيانجا

﴿فأخرج لهم عجلا جسدا له خوار فقالوا هذا إلهكم وإله موسى فنسي﴾ [طه: 88]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo adawatulutsira (kuchokera m’golide wosungunukayo) mwana wang’ombe wokhala ndi thupi lokwanira, yemwe amatulutsa mawu (ngati kulira kwa ng’ombe), (iwo) adati: “Uyu ndi mulungu wanu ndiponso mulungu wa Mûsa, koma (Mûsa) wamuiwala, (choncho wapita kukamfuna ku phiri)!”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek