×

Ngati wina aganiza kuti Mulungu sadzathandiza Mtumwi wake m’dziko lino ndi m’dziko 22:15 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hajj ⮕ (22:15) ayat 15 in Chichewa

22:15 Surah Al-hajj ayat 15 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hajj ayat 15 - الحج - Page - Juz 17

﴿مَن كَانَ يَظُنُّ أَن لَّن يَنصُرَهُ ٱللَّهُ فِي ٱلدُّنۡيَا وَٱلۡأٓخِرَةِ فَلۡيَمۡدُدۡ بِسَبَبٍ إِلَى ٱلسَّمَآءِ ثُمَّ لۡيَقۡطَعۡ فَلۡيَنظُرۡ هَلۡ يُذۡهِبَنَّ كَيۡدُهُۥ مَا يَغِيظُ ﴾
[الحج: 15]

Ngati wina aganiza kuti Mulungu sadzathandiza Mtumwi wake m’dziko lino ndi m’dziko limene lili nkudza, mulekeni amange chingwe ku phaso la nyumba yake ndi kudzimangirira yekha. Ndipo mulekeni kuti awone yekha ngati cholinga chake chingachotse vuto lomwe limamukwiyitsa iye

❮ Previous Next ❯

ترجمة: من كان يظن أن لن ينصره الله في الدنيا والآخرة فليمدد بسبب, باللغة نيانجا

﴿من كان يظن أن لن ينصره الله في الدنيا والآخرة فليمدد بسبب﴾ [الحج: 15]

Khaled Ibrahim Betala
“Amene akuganiza kuti Allah samthangata (Mtumiki Wake) pa dziko lapansi ndi patsiku la chimaliziro, amange chingwe kudenga, kenako adzipachike (ngati safuna kuona Chisilamu chikufala); ndipo aone kuti kodi ndale zakezo zichotsa zimene zamkwiitsazo
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek