×

Kuti adzaona zinthu zimene zili zaphindu kwa iwo ndi kutchula dzina la 22:28 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hajj ⮕ (22:28) ayat 28 in Chichewa

22:28 Surah Al-hajj ayat 28 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hajj ayat 28 - الحج - Page - Juz 17

﴿لِّيَشۡهَدُواْ مَنَٰفِعَ لَهُمۡ وَيَذۡكُرُواْ ٱسۡمَ ٱللَّهِ فِيٓ أَيَّامٖ مَّعۡلُومَٰتٍ عَلَىٰ مَا رَزَقَهُم مِّنۢ بَهِيمَةِ ٱلۡأَنۡعَٰمِۖ فَكُلُواْ مِنۡهَا وَأَطۡعِمُواْ ٱلۡبَآئِسَ ٱلۡفَقِيرَ ﴾
[الحج: 28]

Kuti adzaona zinthu zimene zili zaphindu kwa iwo ndi kutchula dzina la Mulungu, pa masiku osankhidwa, pa nyama ya ng’ombe imene Iye wawapatsa iwo. Idyani gawo lina ndiponso dyetsani osauka amene ali pa mavuto

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ليشهدوا منافع لهم ويذكروا اسم الله في أيام معلومات على ما رزقهم, باللغة نيانجا

﴿ليشهدوا منافع لهم ويذكروا اسم الله في أيام معلومات على ما رزقهم﴾ [الحج: 28]

Khaled Ibrahim Betala
“Kuti adzaone zabwino zawo, ndikuti (achulukitse) kutchula dzina la Allah m’masiku odziwika (ubwino wake), kupyolera m’zimene wawapatsa monga ziweto za miyendo inayi. Ndipo idyani ina mwa nyamayo ndi kum’dyetsa wovutika, wosauka
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek