×

Ndipo pamene chivumbulutso chathu chomveka chilakatulidwa kwa iwo, iwe udzaona kukana pa 22:72 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hajj ⮕ (22:72) ayat 72 in Chichewa

22:72 Surah Al-hajj ayat 72 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hajj ayat 72 - الحج - Page - Juz 17

﴿وَإِذَا تُتۡلَىٰ عَلَيۡهِمۡ ءَايَٰتُنَا بَيِّنَٰتٖ تَعۡرِفُ فِي وُجُوهِ ٱلَّذِينَ كَفَرُواْ ٱلۡمُنكَرَۖ يَكَادُونَ يَسۡطُونَ بِٱلَّذِينَ يَتۡلُونَ عَلَيۡهِمۡ ءَايَٰتِنَاۗ قُلۡ أَفَأُنَبِّئُكُم بِشَرّٖ مِّن ذَٰلِكُمُۚ ٱلنَّارُ وَعَدَهَا ٱللَّهُ ٱلَّذِينَ كَفَرُواْۖ وَبِئۡسَ ٱلۡمَصِيرُ ﴾
[الحج: 72]

Ndipo pamene chivumbulutso chathu chomveka chilakatulidwa kwa iwo, iwe udzaona kukana pa maso pa anthu osakhulupirira! Iwo ali pafupifupi kumenyana ndi iwo amene amalakatula chivumbulutso chathu kwa iwo. Nena “Kodi mufuna ndikuuzeni zoipa kuposa chizindikiro choterechi? Chizindikirocho ndi moto wa ku Gahena umene Mulungu walonjeza anthu osakhulupirira ndipo amenewa ndi malo oipa kupitako.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإذا تتلى عليهم آياتنا بينات تعرف في وجوه الذين كفروا المنكر يكادون, باللغة نيانجا

﴿وإذا تتلى عليهم آياتنا بينات تعرف في وجوه الذين كفروا المنكر يكادون﴾ [الحج: 72]

Khaled Ibrahim Betala
“Koma Ayah Zathu zomveka zikawerengedwa kwa iwo, uona kunyansidwa pankhope za amene sadakhulupirire. Ndipo amakhala pafupi kuwamenya amene amawawerengera Ayah Zathu. Nena: “Kodi ndikuuzeni zoipa kwambiri kuposa izi? Ndi Moto (wa Allah) umene wawalonjeza amene sadakhulupirire (Allah ndi Mtumiki Wake) amenewo ndi mabwelero oipa zedi.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek