×

Munthu wotere amathyola khosi monyadira ndi kusocheza ena ku njira ya Mulungu. 22:9 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hajj ⮕ (22:9) ayat 9 in Chichewa

22:9 Surah Al-hajj ayat 9 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hajj ayat 9 - الحج - Page - Juz 17

﴿ثَانِيَ عِطۡفِهِۦ لِيُضِلَّ عَن سَبِيلِ ٱللَّهِۖ لَهُۥ فِي ٱلدُّنۡيَا خِزۡيٞۖ وَنُذِيقُهُۥ يَوۡمَ ٱلۡقِيَٰمَةِ عَذَابَ ٱلۡحَرِيقِ ﴾
[الحج: 9]

Munthu wotere amathyola khosi monyadira ndi kusocheza ena ku njira ya Mulungu. Kwa otere kuli mnyozo m’moyo uno ndipo patsiku louka kwa akufa, tidzamulawitsa chilango cha moto woyaka

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ثاني عطفه ليضل عن سبيل الله له في الدنيا خزي ونذيقه يوم, باللغة نيانجا

﴿ثاني عطفه ليضل عن سبيل الله له في الدنيا خزي ونذيقه يوم﴾ [الحج: 9]

Khaled Ibrahim Betala
“(Yemwe) akupinda khosi lake (chifukwa chodzikuza) kuti asokereze (anthu powachotsa) kunjira ya Allah; pa iye pali chilango choyalutsa pa moyo uno, ndipo patsiku la Qiyâma tikamulawitsa chilango cha Moto wotentha
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek