×

Pamenemudamvankhaniyi, bwanjianthuokhulupirira, amuna ndi akazi, sadafune kuganizira zabwino za anthu awo ndi 24:12 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nur ⮕ (24:12) ayat 12 in Chichewa

24:12 Surah An-Nur ayat 12 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nur ayat 12 - النور - Page - Juz 18

﴿لَّوۡلَآ إِذۡ سَمِعۡتُمُوهُ ظَنَّ ٱلۡمُؤۡمِنُونَ وَٱلۡمُؤۡمِنَٰتُ بِأَنفُسِهِمۡ خَيۡرٗا وَقَالُواْ هَٰذَآ إِفۡكٞ مُّبِينٞ ﴾
[النور: 12]

Pamenemudamvankhaniyi, bwanjianthuokhulupirira, amuna ndi akazi, sadafune kuganizira zabwino za anthu awo ndi kunena kuti, “Ili ndi bodza loonekera poyera?”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: لولا إذ سمعتموه ظن المؤمنون والمؤمنات بأنفسهم خيرا وقالوا هذا إفك مبين, باللغة نيانجا

﴿لولا إذ سمعتموه ظن المؤمنون والمؤمنات بأنفسهم خيرا وقالوا هذا إفك مبين﴾ [النور: 12]

Khaled Ibrahim Betala
“Nanga bwanji pamene mudaimva (nkhani) iyi okhulupirira achimuna ndi okhulupirira achikazi saadaganizire anzawo zabwino ndikunena kuti: “Ili ndi bodza loonekera?”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek