×

Munthu wamkazi wosakwatiwa akachita chigololo ndi munthu wamwamuna wosakwatira, mukwapule aliyense wa 24:2 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nur ⮕ (24:2) ayat 2 in Chichewa

24:2 Surah An-Nur ayat 2 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nur ayat 2 - النور - Page - Juz 18

﴿ٱلزَّانِيَةُ وَٱلزَّانِي فَٱجۡلِدُواْ كُلَّ وَٰحِدٖ مِّنۡهُمَا مِاْئَةَ جَلۡدَةٖۖ وَلَا تَأۡخُذۡكُم بِهِمَا رَأۡفَةٞ فِي دِينِ ٱللَّهِ إِن كُنتُمۡ تُؤۡمِنُونَ بِٱللَّهِ وَٱلۡيَوۡمِ ٱلۡأٓخِرِۖ وَلۡيَشۡهَدۡ عَذَابَهُمَا طَآئِفَةٞ مِّنَ ٱلۡمُؤۡمِنِينَ ﴾
[النور: 2]

Munthu wamkazi wosakwatiwa akachita chigololo ndi munthu wamwamuna wosakwatira, mukwapule aliyense wa iwo zikoti zana limodzi ndipo musalole kuti chifundo chikulepheretseni kumvera lamulo la Mulungu ngati inu mumakhulupirira mwa Mulungu ndi tsiku lomaliza. Ndipo onetsetsani kuti chilango chawo chachitidwa umboni ndi anthu ambiri okhulupirira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: الزانية والزاني فاجلدوا كل واحد منهما مائة جلدة ولا تأخذكم بهما رأفة, باللغة نيانجا

﴿الزانية والزاني فاجلدوا كل واحد منهما مائة جلدة ولا تأخذكم بهما رأفة﴾ [النور: 2]

Khaled Ibrahim Betala
“Mkazi wachiwerewere ndi mwamuna wa chiwerewere aliyense wa iwo mkwapuleni zikoti zana limodzi . Musagwidwe chisoni ndi iwo pa chipembedzo (malamulo) cha Allah, ngati inu mukukhulupiriradi mwa Allah ndi tsiku la chimaliziro. Ndipo gulu la okhulupirira lionelere chilango chawo
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek