×

Mwamuna wachigololo asakwatire wina koma mkazi wachigololo kapena mkazi wopembedza mafano. Mkazi 24:3 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nur ⮕ (24:3) ayat 3 in Chichewa

24:3 Surah An-Nur ayat 3 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nur ayat 3 - النور - Page - Juz 18

﴿ٱلزَّانِي لَا يَنكِحُ إِلَّا زَانِيَةً أَوۡ مُشۡرِكَةٗ وَٱلزَّانِيَةُ لَا يَنكِحُهَآ إِلَّا زَانٍ أَوۡ مُشۡرِكٞۚ وَحُرِّمَ ذَٰلِكَ عَلَى ٱلۡمُؤۡمِنِينَ ﴾
[النور: 3]

Mwamuna wachigololo asakwatire wina koma mkazi wachigololo kapena mkazi wopembedza mafano. Mkazi wachigololo asakwatiwe ndi wina koma mwamuna wachigololo kapena wopembedza mafano. Anthu okhulupirira moona saloledwa maukwati otere

❮ Previous Next ❯

ترجمة: الزاني لا ينكح إلا زانية أو مشركة والزانية لا ينكحها إلا زان, باللغة نيانجا

﴿الزاني لا ينكح إلا زانية أو مشركة والزانية لا ينكحها إلا زان﴾ [النور: 3]

Khaled Ibrahim Betala
“Mwamuna wa chiwerewere sakwatira mkazi (wabwino) koma wachiwerewere mnzake, kapena mkazi wopembedza mafano. Nayenso mkazi wachiwerewere sakwatiwa ndi mwamuna (wabwino) koma wachiwerewere mnzake, kapena wopembedza mafano. Ndipo zimenezi zaletsedwa kwa okhulupirira
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek