×

Ndipo tidamubweretsa iye kwa Amayi ake kuti asangalale, asiye kudandaula ndiponso kuti 28:13 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Qasas ⮕ (28:13) ayat 13 in Chichewa

28:13 Surah Al-Qasas ayat 13 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Qasas ayat 13 - القَصَص - Page - Juz 20

﴿فَرَدَدۡنَٰهُ إِلَىٰٓ أُمِّهِۦ كَيۡ تَقَرَّ عَيۡنُهَا وَلَا تَحۡزَنَ وَلِتَعۡلَمَ أَنَّ وَعۡدَ ٱللَّهِ حَقّٞ وَلَٰكِنَّ أَكۡثَرَهُمۡ لَا يَعۡلَمُونَ ﴾
[القَصَص: 13]

Ndipo tidamubweretsa iye kwa Amayi ake kuti asangalale, asiye kudandaula ndiponso kuti adziwe kuti lonjezo la Mulungu ndi loona. Koma anthu ambiri sachidziwa chimenechi

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فرددناه إلى أمه كي تقر عينها ولا تحزن ولتعلم أن وعد الله, باللغة نيانجا

﴿فرددناه إلى أمه كي تقر عينها ولا تحزن ولتعلم أن وعد الله﴾ [القَصَص: 13]

Khaled Ibrahim Betala
“Choncho tidamubwezera kwa mayi wake kuti maso ake atonthole, (mtima wake ukhazikike) ndi kuti asadandaule; ndi kuti adziwe kuti lonjezo la Allah ndi loona. Koma ambiri a iwo sadziwa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek