×

Farawo adati, “oh inu mafumu! Inu mulibe mulungu wina amene ine ndimudziwa 28:38 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Qasas ⮕ (28:38) ayat 38 in Chichewa

28:38 Surah Al-Qasas ayat 38 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Qasas ayat 38 - القَصَص - Page - Juz 20

﴿وَقَالَ فِرۡعَوۡنُ يَٰٓأَيُّهَا ٱلۡمَلَأُ مَا عَلِمۡتُ لَكُم مِّنۡ إِلَٰهٍ غَيۡرِي فَأَوۡقِدۡ لِي يَٰهَٰمَٰنُ عَلَى ٱلطِّينِ فَٱجۡعَل لِّي صَرۡحٗا لَّعَلِّيٓ أَطَّلِعُ إِلَىٰٓ إِلَٰهِ مُوسَىٰ وَإِنِّي لَأَظُنُّهُۥ مِنَ ٱلۡكَٰذِبِينَ ﴾
[القَصَص: 38]

Farawo adati, “oh inu mafumu! Inu mulibe mulungu wina amene ine ndimudziwa kupatula ine ndekha. Haman, ndipangireni ine njerwa zadothi ndipo mundimangire nyumba yaitali, yonga nsanja, kuti ndikwerepo kupita kwa Mulungu wa Mose. Ndithudi ine ndili kumuganizira kuti Mose ndi mmodzi mwa anthu abodza.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وقال فرعون ياأيها الملأ ما علمت لكم من إله غيري فأوقد لي, باللغة نيانجا

﴿وقال فرعون ياأيها الملأ ما علمت لكم من إله غيري فأوقد لي﴾ [القَصَص: 38]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo Farawo adati: “E inu nduna (zanga)! Sindidziwa kuti inu muli ndi mulungu (wina) kupatula ine. Choncho, iwe Haamana! Ndiwotchere njerwa tero undimangire chipilala kuti mwina mwake ndingamsuzumire Mulungu wa Mûsa. Ndithu ine ndikumganizira kuti ndi mmodzi wa abodza.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek