×

Kodi anthu awiriwa ndi ofanana? Iye amene tamulonjeza lonjezo labwino ndipo adzalikwaniritsa 28:61 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Qasas ⮕ (28:61) ayat 61 in Chichewa

28:61 Surah Al-Qasas ayat 61 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Qasas ayat 61 - القَصَص - Page - Juz 20

﴿أَفَمَن وَعَدۡنَٰهُ وَعۡدًا حَسَنٗا فَهُوَ لَٰقِيهِ كَمَن مَّتَّعۡنَٰهُ مَتَٰعَ ٱلۡحَيَوٰةِ ٱلدُّنۡيَا ثُمَّ هُوَ يَوۡمَ ٱلۡقِيَٰمَةِ مِنَ ٱلۡمُحۡضَرِينَ ﴾
[القَصَص: 61]

Kodi anthu awiriwa ndi ofanana? Iye amene tamulonjeza lonjezo labwino ndipo adzalikwaniritsa ndi iye amene tamupatsa zokoma zambiri za m’moyo uno koma pa tsiku lachiweruzo adzakhala m’gulu la iwo olangidwa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: أفمن وعدناه وعدا حسنا فهو لاقيه كمن متعناه متاع الحياة الدنيا ثم, باللغة نيانجا

﴿أفمن وعدناه وعدا حسنا فهو لاقيه كمن متعناه متاع الحياة الدنيا ثم﴾ [القَصَص: 61]

Khaled Ibrahim Betala
“Kodi munthu yemwe tamulonjeza lonjezo labwino (kuti akalowa ku Munda wamtendere) kotero kuti iye akakumana nalo (lonjezolo), angafanane ndi yemwe tamsangalatsa ndi zosangalatsa za moyo wa pa dziko basi, kenako iye nkukhala mmodzi okaponyedwa (ku Moto) tsiku la chiweruziro (Qiyâma)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek