×

Nena, “Ndiuzeni! Ngati Mulungu atapanga usana kuti kusade mpaka pa tsiku louka 28:72 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Qasas ⮕ (28:72) ayat 72 in Chichewa

28:72 Surah Al-Qasas ayat 72 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Qasas ayat 72 - القَصَص - Page - Juz 20

﴿قُلۡ أَرَءَيۡتُمۡ إِن جَعَلَ ٱللَّهُ عَلَيۡكُمُ ٱلنَّهَارَ سَرۡمَدًا إِلَىٰ يَوۡمِ ٱلۡقِيَٰمَةِ مَنۡ إِلَٰهٌ غَيۡرُ ٱللَّهِ يَأۡتِيكُم بِلَيۡلٖ تَسۡكُنُونَ فِيهِۚ أَفَلَا تُبۡصِرُونَ ﴾
[القَصَص: 72]

Nena, “Ndiuzeni! Ngati Mulungu atapanga usana kuti kusade mpaka pa tsiku louka kwa akufa, kodi ndi mulungu uti kupatula Mulungu weniweni amene akhoza kukupatsani usiku umene inu mumapumulamo? Kodi inu simukuona?”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قل أرأيتم إن جعل الله عليكم النهار سرمدا إلى يوم القيامة من, باللغة نيانجا

﴿قل أرأيتم إن جعل الله عليكم النهار سرمدا إلى يوم القيامة من﴾ [القَصَص: 72]

Khaled Ibrahim Betala
“Nena: “Tandiuzani ngati Allah ataupanga usana kuti usachoke mpaka tsiku la chiweruziro (Qiyâma), kodi ndimulungu wanji osati Allah amene angakudzetsereni usiku m’mene mumapumulamo? Kodi simuona (chifundo cha Allah)?”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek