×

Kotero iye adapita kwa anthu ake monyadira atavala bwino. Anthu amene adali 28:79 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Qasas ⮕ (28:79) ayat 79 in Chichewa

28:79 Surah Al-Qasas ayat 79 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Qasas ayat 79 - القَصَص - Page - Juz 20

﴿فَخَرَجَ عَلَىٰ قَوۡمِهِۦ فِي زِينَتِهِۦۖ قَالَ ٱلَّذِينَ يُرِيدُونَ ٱلۡحَيَوٰةَ ٱلدُّنۡيَا يَٰلَيۡتَ لَنَا مِثۡلَ مَآ أُوتِيَ قَٰرُونُ إِنَّهُۥ لَذُو حَظٍّ عَظِيمٖ ﴾
[القَصَص: 79]

Kotero iye adapita kwa anthu ake monyadira atavala bwino. Anthu amene adali kukonda moyo wa pa dziko lapansi adati, “Tikadakhala kuti tidali nazo ngati zinthu zimene zili ndi Karuni! Ndithudi iye ndi wolemera kwambiri.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فخرج على قومه في زينته قال الذين يريدون الحياة الدنيا ياليت لنا, باللغة نيانجا

﴿فخرج على قومه في زينته قال الذين يريدون الحياة الدنيا ياليت لنا﴾ [القَصَص: 79]

Khaled Ibrahim Betala
“Choncho, adatulukira kwa anthu ake (monyada) uku atadzikongoletsa. Amene akufuna moyo wa pa dziko adanena (mokhumbira): “Kalanga ife! Tikadapatsidwa monga wapatsidwa Qaruna! Ndithu iye ngodala kwakukulu.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek